Genesis 1:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Mulungu anatcha kuyerako Usana, ndi mdimawo anautcha Usiku. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku loyamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Mulungu anacha kuyerako Usana, ndi mdimawo anautcha Usiku. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku loyamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kuyerako adakutcha Usana, mdima uja adautcha Usiku. Ndipo kudali madzulo ndiponso m'maŵa, tsiku loyamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mulungu anatcha kuwalako “usana” ndipo mdima anawutcha “usiku.” Ndipo panali madzulo ndiponso mmawa pa tsiku loyamba. Onani mutuwo |