Genesis 1:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anaona Mulungu kuti kuyerako kunali kwabwino; ndipo Mulungu analekanitsa kuyera ndi mdima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anaona Mulungu kuti kuyerako kunali kwabwino; ndipo Mulungu analekanitsa kuyera ndi mdima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mulungu adaona kuti kuyerako kunali kwabwino. Pomwepo adalekanitsa kuyerako ndi mdima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mulungu anaona kuti kuwalako kunali bwino ndipo Iye analekanitsa kuwala ndi mdima. Onani mutuwo |