Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 150:1 - Buku Lopatulika

1 Aleluya. Lemekezani Mulungu m'malo ake oyera; mlemekezeni m'thambo la mphamvu yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Aleluya. Lemekezani Mulungu m'malo ake oyera; mlemekezeni m'thambo la mphamvu yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tamandani Chauta! Tamandani Mulungu m'malo ake opatulika. Mtamandeni ku thambo lake lamphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 150:1
13 Mawu Ofanana  

Pakuti anapenya pansi ali kumwamba kuli malo ake opatulika; Yehova pokhala kumwamba anapenya dziko lapansi;


Kwezani manja anu kumalo oyera, nimulemekeze Yehova.


Aleluya, Muimbireni Yehova nyimbo yatsopano, ndi chilemekezo chake mu msonkhano wa okondedwa ake.


Zakumwamba zimalalikira ulemerero wa Mulungu; ndipo thambo lionetsa ntchito ya manja ake.


Usana ndi usana uchulukitsa mau, ndipo usiku ndi usiku uonetsa nzeru.


Liu la Yehova liswetsa nyama zazikazi, ndipo lipulula nkhalango; ndipo mu Kachisi mwake zonse zili m'mwemo zimati, Ulemerero.


Ndipo ndinapenya, ndipo taonani, kuthambo lokhala pamwamba pa mitu ya akerubi kudaoneka ngati mwala wasafiro, ngati maonekedwe a chifaniziro cha mpando wachifumu pamwamba pao.


Ndipo aphunzitsi adzawala ngati kunyezimira kwa thambo; ndi iwo otembenuza ambiri atsate chilungamo ngati nyenyezi kunthawi za nthawi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa