Masalimo 150:1 - Buku Lopatulika1 Aleluya. Lemekezani Mulungu m'malo ake oyera; mlemekezeni m'thambo la mphamvu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Aleluya. Lemekezani Mulungu m'malo ake oyera; mlemekezeni m'thambo la mphamvu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tamandani Chauta! Tamandani Mulungu m'malo ake opatulika. Mtamandeni ku thambo lake lamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu. Onani mutuwo |