Masalimo 8:4 - Buku Lopatulika4 munthu ndani kuti mumkumbukira? Ndi mwana wa munthu kuti mucheza naye? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 munthu ndani kuti mumkumbukira? Ndi mwana wa munthu kuti mucheza naye? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 ndimadzifunsa kuti, “Kodi munthu nchiyani kuti muzimkumbukira, mwana wa munthu nchiyani kuti muzimsamalira?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye? Onani mutuwo |