Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 19:3 - Buku Lopatulika

3 Palibe chilankhulidwe, palibe mau; liu lao silimveka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Palibe chilankhulidwe, palibe mau; liu lao silimveka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Palibe kulankhula, palibe kunena mau aliwonse. Liwu lao silimveka konse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse; liwu lawo silimveka.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 19:3
1 Mawu Ofanana  

ndi kuti mungakweze maso anu kupenya kumwamba, ndipo poona dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi, khamu lonse la kumwamba, munganyengedwe ndi kuzigwadira, ndi kuzitumikira, zimene Yehova Mulungu wanu anagawira mitundu yonse ya anthu pansi pa thambo lonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa