Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:6 - Buku Lopatulika

Zingwe za kumanda zinandizingira; misampha ya imfa inandifikira ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zingwe za kumanda zinandizingira; misampha ya imfa inandifikira ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthambo zakumanda zidandizeŵeza, misampha ya imfa idandikola.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:6
10 Mawu Ofanana  

Ndipo akamangidwa m'nsinga, nakakodwa ndi zingwe za mazunzo,


Zingwe za imfa zinandizinga, ndi zowawa za manda zinandigwira: ndinapeza nsautso ndi chisoni.


Odzikuza ananditchera msampha, nandibisira zingwe; anatcha ukonde m'mphepete mwa njira; ananditchera makwekwe.


Zingwe za manda zindizinga, misampha ya imfa inandifikira ine.


Malamulo a wanzeru ndiwo kasupe wa moyo, apatutsa kumisampha ya imfa.


Kuopa Yehova ndiko kasupe wa moyo, kupatutsa kumisampha ya imfa.


Zoipa zakezake zidzagwira woipa; adzamangidwa ndi zingwe za uchimo wake.


Ndipo anati, Ndinaitana Yehova m'nsautso wanga, ndipo anandiyankha ine; ndinafuula ndili m'mimba ya manda, ndipo munamva mau anga.


Koma pamene paliponse mudzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu a ankhondo, zindikirani pamenepo kuti chipulumutso chake chayandikira.


yemweyo Mulungu anamuukitsa, atamasula zowawa za imfa, mwakuti sikunali kotheka kuti Iye agwidwe nayo.