Machitidwe a Atumwi 2:24 - Buku Lopatulika24 yemweyo Mulungu anamuukitsa, atamasula zowawa za imfa, mwakuti sikunali kotheka kuti Iye agwidwe nayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 yemweyo Mulungu anamuukitsa, atamasula zowawa za imfa, mwakuti sikunali kotheka kuti Iye agwidwe nayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma Mulungu adammasula ku zoŵaŵa za imfa, namuukitsa kwa akufa, chifukwa kunali kosatheka kuti agonjetsedwe ndi imfa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Mulungu anamuukitsa kwa akufa, kumumasula Iye ku zowawa za imfa, chifukwa kunali kosatheka kuti agwiridwe ndi imfa. Onani mutuwo |