Luka 21:20 - Buku Lopatulika20 Koma pamene paliponse mudzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu a ankhondo, zindikirani pamenepo kuti chipulumutso chake chayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma pamene paliponse mudzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu a ankhondo, zindikirani pamenepo kuti chipulumutso chake chayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Pamene mudzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu a ankhondo, dziŵani kuti chiwonongeko chake chafika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Mukadzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu ankhondo, inu mudzadziwe kuti kuwonongeka kwake kuli pafupi. Onani mutuwo |