Yona 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anati, Ndinaitana Yehova m'nsautso wanga, ndipo anandiyankha ine; ndinafuula ndili m'mimba ya manda, ndipo munamva mau anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anati, Ndinaitana Yehova m'nsautso yanga, ndipo anandiyankha ine; ndinafuula ndili m'mimba ya manda, ndipo munamva mau anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adati, “Inu Chauta, pamene ndinali m'mavuto ndidakuitanani, ndipo mudandiyankha. Pamene ndinali m'dziko la akufa ndidalira kwa Inu kuti mundithandize, ndipo mudamva pempho langa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. Onani mutuwo |