Yona 2:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo Yona anapemphera kwa Yehova Mulungu wake ali m'mimba mwa nsombayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo Yona anapemphera kwa Yehova Mulungu wake ali m'mimba mwa nsombayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Yona ali m'mimba mwa chinsomba chija, adayamba kutama Chauta mopemba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake. Onani mutuwo |