Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 71:12 - Buku Lopatulika

Musandikhalire kutali, Mulungu; fulumirani kundithandiza, Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Musandikhalire kutali, Mulungu; fulumirani kundithandiza, Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, musandikhalire kutali. Inu Mulungu wanga, fulumirani kudzandithandiza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musakhale kutali ndi ine Inu Mulungu, bwerani msanga, Inu Mulungu wanga; thandizeni.

Onani mutuwo



Masalimo 71:12
10 Mawu Ofanana  

Muimiranji patali, Yehova? Mubisaliranji m'nyengo za nsautso?


Fulumirani ndiyankheni, Yehova; mzimu wanga ukutha. Musandibisire nkhope yanu; ndingafanane nao akutsikira kudzenje.


Musandikhalire kutali; pakuti nsautso ili pafupi, pakuti palibe mthandizi.


Koma Inu, Yehova, musakhale kutali; mphamvu yanga Inu, mufulumire kundithandiza.


Yehova, mudazipenya; musakhale chete, Ambuye, musakhale kutali ndi ine.


Ndikupemphani, Yehova, ndilanditseni; fulumirani kudzandithandiza, Yehova.


Yandikizani moyo wanga, ndi kuuombola; ndipulumutseni chifukwa cha adani anga.


Koma ine ndine wozunzika ndi waumphawi; mundifulumirire, Mulungu. Inu ndinu mthandizi wanga ndi Mpulumutsi wanga; musachedwe, Yehova.