Masalimo 143:7 - Buku Lopatulika7 Fulumirani ndiyankheni, Yehova; mzimu wanga ukutha. Musandibisire nkhope yanu; ndingafanane nao akutsikira kudzenje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Fulumirani ndiyankheni, Yehova; mzimu wanga ukutha. Musandibisire nkhope yanu; ndingafanane nao akutsikira kudzenje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Fulumirani kundiyankha, Inu Chauta. Ndataya mtima kwambiri, musandibisire nkhope yanu, kuti ndingafanefane ndi anthu otsikira ku manda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yehova ndiyankheni msanga; mzimu wanga ukufowoka. Musandibisire nkhope yanu, mwina ndidzakhala ngati iwo amene atsikira ku dzenje. Onani mutuwo |