Masalimo 10:1 - Buku Lopatulika1 Muimiranji patali, Yehova? Mubisaliranji m'nyengo za nsautso? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Muimiranji patali, Yehova? Mubisaliranji m'nyengo za nsautso? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chifukwa chiyani mumaima kutali nafe, Inu Chauta? Chifukwa chiyani mumabisala pamene tili pa mavuto? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nʼchifukwa chiyani Yehova mwayima patali? Chifukwa chiyani mukudzibisa nokha pa nthawi ya mavuto? Onani mutuwo |