Masalimo 9:20 - Buku Lopatulika20 Muwachititse mantha, Yehova; adziwe amitundu kuti ali anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Muwachititse mantha, Yehova; adziwe amitundu kuti ali anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Inu Chauta, aopseni anthuwo. Akunjawo adziŵe kuti iwo ndi anthu chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Akantheni ndi mantha aakulu, Inu Yehova; mitundu idziwe kuti iwo ndi anthu wamba. Sela Onani mutuwo |