Masalimo 22:19 - Buku Lopatulika19 Koma Inu, Yehova, musakhale kutali; mphamvu yanga Inu, mufulumire kundithandiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Inu, Yehova, musakhale kutali; mphamvu yanga Inu, mufulumire kundithandiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma Inu Chauta musakhale kutali. Inu, mphamvu zanga, fulumirani kudzandithandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma Inu Yehova, musakhale kutali; Inu mphamvu yanga, bwerani msanga kuti mudzandithandize. Onani mutuwo |