Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 22:18 - Buku Lopatulika

18 Agawana zovala zanga, nachita maere pa malaya anga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Agawana zovala zanga, nachita maere pa malaya anga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Agaŵana zovala zanga, ndipo achitira malaya anga maere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Iwo agawana zovala zanga pakati pawo ndi kuchita maere pa zovala zangazo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 22:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anampachika Iye, anagawana zovala zake ndi kulota maere:


Ndipo anampachika Iye, nagawana zovala zake mwa iwo okha, ndi kuchita maere pa izo, kuti adziwe yense adzatenga chiyani.


Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa