Masalimo 22:17 - Buku Lopatulika17 Ndikhoza kuwerenga mafupa anga onse; iwo ayang'ana nandipenyetsetsa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndikhoza kuwerenga mafupa anga onse; iwo ayang'ana nandipenyetsetsa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mafupa anga akuwonekera, koma anthu aja akungondiyang'anitsitsa akukondwera poona kuti ndikuvutika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ine nditha kuwerenga mafupa anga onse; anthu amandiyangʼanitsitsa ndi kundidzuma. Onani mutuwo |