Masalimo 22:16 - Buku Lopatulika16 Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Anthu ankhanza andizinga ngati mimbulu. Aboola manja anga ndi mapazi anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Agalu andizungulira; gulu la anthu oyipa landizinga. Alasa manja ndi mapazi anga. Onani mutuwo |