Masalimo 22:15 - Buku Lopatulika15 Mphamvu yanga yauma ngati phale; ndi lilime langa likangamira kunsaya zanga; ndipo mwandifikitsa kufumbi la imfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Mphamvu yanga yauma ngati phale; ndi lilime langa likangamira kunsaya zanga; ndipo mwandifikitsa kufumbi la imfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kukhosi kwanga kwauma ngati phale, lilime langa lakangamira ku nsagwada. Inu mwandisiya pa fumbi kuti ndifere pomwepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mphamvu zanga zauma ngati phale, ndipo lilime langa lamamatira ku nsagwada; mwandigoneka mʼfumbi la imfa. Onani mutuwo |