Masalimo 22:14 - Buku Lopatulika14 Ndathiridwa pansi monga madzi, ndipo mafupa anga onse anaguluka. Mtima wanga ukunga sera; wasungunuka m'kati mwa matumbo anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndathiridwa pansi monga madzi, ndipo mafupa anga onse anaguluka. Mtima wanga ukunga sera; wasungunuka m'kati mwa matumbo anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Moyo wanga watayika ngati madzi, mafupa anga aweyeseka. Mtima wanga uli ngati sera, wasungunuka m'kati mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ine ndatayika pansi ngati madzi ndipo mafupa anga onse achoka mʼmalo mwake. Mtima wanga wasanduka phula; wasungunuka mʼkati mwanga. Onani mutuwo |