Masalimo 22:13 - Buku Lopatulika13 Andiyasamira m'kamwa mwao, ngati mkango wozomola ndi wobangula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Andiyasamira m'kamwa mwao, ngati mkango wozomola ndi wobangula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Andiyasamira kukamwa, ngati mkango wobangula wofuna kundikadzula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mikango yobangula pokadzula nyama, yatsekula kwambiri pakamwa pawo kulimbana nane. Onani mutuwo |