Masalimo 22:12 - Buku Lopatulika12 Ng'ombe zamphongo zambiri zandizinga; mphongo zolimba za ku Basani zandizungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ng'ombe zamphongo zambiri zandizinga; mphongo zolimba za ku Basani zandizungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nkhunzi zambiri zandizungulira. Adani amphamvu ngati nkhunzi za ku Basani andizinga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ngʼombe zazimuna zandizungulira; ngʼombe zazimuna zamphamvu za ku Basani zandizinga. Onani mutuwo |