Masalimo 22:20 - Buku Lopatulika20 Landitsani moyo wanga kulupanga; wokondedwa wanga kumphamvu ya galu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Landitsani moyo wanga kulupanga; wokondedwa wanga kumphamvu ya galu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pulumutsani moyo wanga ku lupanga. Landitseni ku mphamvu za mimbulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Pulumutsani moyo wanga ku lupanga, moyo wanga wopambanawu ku mphamvu ya agalu. Onani mutuwo |