Masalimo 22:21 - Buku Lopatulika21 ndipulumutseni m'kamwa mwa mkango; inde mwandiyankha ine ndili pa nyanga za njati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndipulumutseni m'kamwa mwa mkango; inde mwandiyankha ine ndili pa nyanga za njati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Pulumutseni kukamwa kwa mkango, mulanditse moyo wanga wovutika ku nyanga za njati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Ndilanditseni mʼkamwa mwa mikango; pulumutseni ku nyanga za njati. Onani mutuwo |