Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 64:3 - Buku Lopatulika

Amene anola lilime lao ngati lupanga, napiringidza mivi yao, ndiyo mau akuwawitsa;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amene anola lilime lao ngati lupanga, napiringidza mivi yao, ndiyo mau akuwawitsa;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo amanola lilime lao ngati lupanga, amaponya mau obaya ngati mivi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo amanola malilime awo ngati malupanga, amaponya mawu awo olasa ngati mivi.

Onani mutuwo



Masalimo 64:3
9 Mawu Ofanana  

Pakuti, onani, oipa akoka uta, apiringidza muvi wao pansinga, kuwaponyera mumdima oongoka mtima.


Mundisunge ndisagwe mumsampha ananditcherawo, ndisakodwe m'makwekwe a iwo ochita zopanda pake.


Moyo wanga uli pakati pa mikango; ndigona pakati pa oyaka moto, ndiwo ana a anthu amene mano ao ali nthungo ndi mivi, ndipo lilime lao ndilo lupanga lakuthwa.


Apitetu ngati madzi oyenda; popiringidza mivi yake ikhale yodukaduka.


Alipo wonena mwansontho ngati kupyoza kwa lupanga; koma lilime la anzeru lilamitsa.


Pali mbadwo mano ao akunga malupanga, zibwano zao zikunga mipeni; kuti adye osauka kuwachotsa kudziko, ndi aumphawi kuwachotsa mwa anthu.


Palibe chida chosulidwira iwe chidzapindula; ndipo lilime lonse limene lidzakangana nawe m'chiweruzo udzalitsutsa. Ichi ndi cholowa cha atumiki a Yehova, ndi chilungamo chao chimene chifuma kwa Ine, ati Yehova.


Ndipo apinda lilime lao ngati uta wao, liname; koma akula mphamvu m'dzikomo, koma si pachoonadi; pakuti alinkunkabe nachita zoipa, ndipo sandidziwa Ine, ati Yehova.