Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 58:7 - Buku Lopatulika

7 Apitetu ngati madzi oyenda; popiringidza mivi yake ikhale yodukaduka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Apitetu ngati madzi oyenda; popiringidza mivi yake ikhale yodukaduka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Azimirire ngati madzi opita, mivi yao iŵafotere m'manja ngati udzu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Mulole kuti asowe ngati madzi oyenda pamene iwo akoka uta mulole kuti mivi yawo ikhale yosathwa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 58:7
11 Mawu Ofanana  

Ndipo ngakhale ngwazi imene mtima wake ukunga mtima wa mkango idzasungunuka konse, pakuti Aisraele onse adziwa atate wanu kuti ndiye munthu wamphamvu, ndi iwo ali naye ndiwo ngwazi.


Kubangula kwa mkango, ndi kulira kwa mkango waukali kwaletsedwa, ndi mano a misona ya mkango athyoledwa.


Woipa adzaziona, nadzapsa mtima; adzakukuta mano, nadzasungunuka; chokhumba oipa chidzatayika.


Ndathiridwa pansi monga madzi, ndipo mafupa anga onse anaguluka. Mtima wanga ukunga sera; wasungunuka m'kati mwa matumbo anga.


Chipulumutso ncha Yehova; dalitso lanu likhale pa anthu anu.


Amene anola lilime lao ngati lupanga, napiringidza mivi yao, ndiyo mau akuwawitsa;


Pamenepo mafumu a Edomu anadabwa; agwidwa nako kunthunthumira amphamvu a ku Mowabu; okhala mu Kanani onse asungunuka mtima.


Chifukwa chake manja onse adzafooka, ndi mitima yonse ya anthu idzasungunuka;


Ndipo amuna a ku Ai anawakantha amuna, ngati makumi atatu mphambu asanu ndi mmodzi; nawapirikitsa kuyambira pachipata mpaka ku Sebarimu, nawakantha potsika; ndi mitima ya anthu inasungunuka inga madzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa