Yeremiya 9:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo apinda lilime lao ngati uta wao, liname; koma akula mphamvu m'dzikomo, koma si pachoonadi; pakuti alinkunkabe nachita zoipa, ndipo sandidziwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo apinda lilime lao ngati uta wao, liname; koma akula mphamvu m'dzikomo, koma si pachoonadi; pakuti alinkunkabe nachita zoipa, ndipo sandidziwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Amapinda lilime ngati uta. Dziko ladzaza ndi zabodza osati zoona. “Amanka naonjezeraonjezera zoipa, ndipo sandidziŵa Ine,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Amapinda lilime lawo ngati uta. Mʼdzikomo mwadzaza ndi mabodza okhaokha osati zoonadi. Amapitirirabe kuchita zoyipa; ndipo sandidziwa Ine.” Akutero Yehova. Onani mutuwo |