Yeremiya 9:2 - Buku Lopatulika2 Ha, ndikadakhala ndi chigono cha anthu aulendo m'chipululu; kuti ndisiye anthu anga, ndiwachokere, pakuti onse ali achigololo, msonkhano wa anthu achiwembu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ha, ndikadakhala ndi chigono cha anthu aulendo m'chipululu; kuti ndisiye anthu anga, ndiwachokere, pakuti onse ali achigololo, msonkhano wa anthu achiwembu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndani adzandipatse pogona m'chipululu, kuti ndiŵasiye anthu anga ndi kuŵathaŵa. Paja onsewo ngachigololo, ndiponso ndi gulu la anthu onyenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndani adzandipatsa malo ogona mʼchipululu kuti ndiwasiye anthu anga ndi kuwachokera kupita kutali; pakuti onse ndi achigololo, ndiponso gulu la anthu onyenga. Onani mutuwo |