Masalimo 64:2 - Buku Lopatulika2 Ndibiseni pa upo wachinsinsi wa ochita zoipa; pa phokoso la ochita zopanda pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndibiseni pa upo wachinsinsi wa ochita zoipa; pa phokoso la ochita zopanda pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tchinjirizeni ku upo wachiwembu wa anthu oipa, tetezeni ku chiwawa cha anthu ochita zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa, ku gulu laphokoso la anthu ochita zoyipa. Onani mutuwo |