Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 64:2 - Buku Lopatulika

2 Ndibiseni pa upo wachinsinsi wa ochita zoipa; pa phokoso la ochita zopanda pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndibiseni pa upo wachinsinsi wa ochita zoipa; pa phokoso la ochita zopanda pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Tchinjirizeni ku upo wachiwembu wa anthu oipa, tetezeni ku chiwawa cha anthu ochita zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa, ku gulu laphokoso la anthu ochita zoyipa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 64:2
20 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa Kaini, Ukwiyiranji? Yagweranji nkhope yako?


Mundilanditse kwa adani anga, Yehova; ndibisala mwa Inu.


Adzikhazikitsa mafumu a dziko lapansi, nachita upo akulu pamodzi, Kutsutsana naye Yehova, ndi Wodzozedwa wake, ndi kuti,


Chifukwa kuti pa tsiku la tsoka Iye adzandibisa mumsasa mwake, adzandibisa mkati mwa chihema chake; pathanthwe adzandikweza.


Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri.


Pobisalira pamaso panu mudzawabisa kwa chiwembu cha munthu, mudzawabisa iwo mumsasa kuti muwalanditse pa kutetana kwa malilime.


Amemezana, alalira, atchereza mapazi anga, popeza alindira moyo wanga.


Mundilanditse kwa ochita zopanda pake, ndipo ndipulumutseni kwa anthu olira mwazi.


Ndipo munthu adzakhala monga pobisalira mphepo, ndi pousira chimphepo; monga mitsinje yamadzi m'malo ouma, monga mthunzi wa thanthwe lalikulu m'dziko lotopetsa.


Koma ine ndinanga mwanawankhosa wofatsa wotengedwa kukaphedwa; ndipo sindinadziwe kuti anandichitira ine chiwembu, kuti, Tiononge mtengo ndi zipatso zake, timdule iye padziko la amoyo, kuti dzina lake lisakumbukikenso.


Mundimvere ine, Yehova, mumve mau a iwo akulimbana ndi ine.


Koma, Yehova, mudziwa uphungu wao wonse wakundinenera ine kundipha ine; musakhulukire mphulupulu yao, musafafanize tchimo lao pamaso panu; aphunthwitsidwe pamaso panu; muchite nao m'nthawi ya mkwiyo wanu.


Ndipo Ayudanso anavomerezana naye, natsimikiza kuti izi zitero.


nampempha kuti mlandu wake wa Paulo uipe, kuti amuitane iye adze ku Yerusalemu; iwo amchitira chifwamba kuti amuphe panjira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa