Masalimo 64:1 - Buku Lopatulika1 Imvani Mulungu, mau anga, m'kudandaula kwanga; sungani moyo wanga angandiopse mdani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Imvani Yehova, mau anga, m'kudandaula kwanga; sungani moyo wanga angandiopse mdani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Imvani mau anga, Inu Mulungu, pamene ndikukudandaulirani. Tetezani moyo wanga kwa mdani woopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga; tetezani moyo wanga ku chiopsezo cha mdani. Onani mutuwo |