Masalimo 64:4 - Buku Lopatulika4 kuponyera wangwiro mobisika: Amponyera modzidzimutsa, osaopa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kuponyera wangwiro mobisika: Amponyera modzidzimutsa, osaopa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amabisalira anthu osalakwa namaŵalasa modzidzimutsa ndi mopanda mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa; amamulasa modzidzimutsa ndi mopanda mantha. Onani mutuwo |