Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 48:9 - Buku Lopatulika

Tidalingalira zachifundo chanu, Mulungu, m'kati mwa Kachisi wanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tidalingalira zachifundo chanu, Mulungu, m'kati mwa Kachisi wanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tikakhala m'Nyumba mwanu, Inu Mulungu, timalingalira za chikondi chanu chosasinthika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.

Onani mutuwo



Masalimo 48:9
14 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa mfumu, Idali yoonadi mbiri ija ndinaimva ine ku dziko langa ya machitidwe anu ndi nzeru zanu.


Koma sindinakhulupirire mau amenewo mpaka ndafika ine kuno, ndaona ndi maso anga; ndipo taonani, anangondiuza dera lina lokha; nzeru zanu ndi zokoma zanu zakula pa mbiri ndinaimvayo.


Pomlingirira Iye pandikonde; ndidzakondwera mwa Yehova.


Pakuti chifundo chanu chili pamaso panga; ndipo ndayenda m'choona chanu.


Chilungamo chanu sindinachibise m'kati mwamtima mwanga; chikhulupiriko chanu ndi chipulumutso chanu ndinachinena; chifundo chanu ndi choonadi chanu sindinachibisire msonkhano waukulu.


Ndipo adzanena za Ziyoni, uyu ndi uyo anabadwa m'mwemo; ndipo Wam'mwambamwamba ndiye adzaukhazikitsa.


Undikoke; tikuthamangire; mfumu yandilowetsa m'zipinda zake: Tidzasangalala ndi kukondwera ndi iwe. Tidzatchula chikondi chako koposa vinyo: Akukonda molungama.


Inde m'njira ya maweruziro anu, Yehova, ife talindira Inu; moyo wathu ukhumba dzina lanu, ndi chikumbukiro chanu.


Ndipo chigwa chonse cha mitembo, ndi cha phulusa, ndi minda yonse kufikira kumtsinje wa Kidroni, kufikira kungodya kwa Chipata cha Akavalo kuloza kum'mawa, ponsepo padzapatulikira Yehova; sipadzazulidwa, sipadzagwetsedwa konse kunthawi zamuyaya.