Masalimo 104:34 - Buku Lopatulika34 Pomlingirira Iye pandikonde; ndidzakondwera mwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Pomlingirira Iye pandikonde; ndidzakondwera mwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Mapemphero anga amkomere Chauta, popeza kuti ndimakondwa mwa Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Zolingalira zanga zikhale zomukomera Iye, pamene ndikusangalala mwa Yehova. Onani mutuwo |