Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 104:34 - Buku Lopatulika

34 Pomlingirira Iye pandikonde; ndidzakondwera mwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Pomlingirira Iye pandikonde; ndidzakondwera mwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Mapemphero anga amkomere Chauta, popeza kuti ndimakondwa mwa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Zolingalira zanga zikhale zomukomera Iye, pamene ndikusangalala mwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:34
18 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anatuluka kulingalira m'munda madzulo; ndipo anatukula maso ake, nayang'ana, taona, ngamira zinalinkudza.


Komatu m'chilamulo cha Yehova muli chikondwerero chake; ndipo m'chilamulo chake amalingirira usana ndi usiku.


Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere.


Ndinalandira mboni zanu zikhale cholandira chosatha; pakuti ndizo zokondweretsa mtima wanga.


Moyo wanga unasamalira mboni zanu; ndipo ndizikonda kwambiri.


Sekerani mwa Yehova, ndimo kondwerani inu olungama mtima; ndipo fuulani mokondwera nonsenu oongoka mtima.


Ndipo moyo wanga udzakondwera mwa Yehova; udzasekera mwa chipulumutso chake.


Ndipo ndidzalingalira ntchito yanu yonse, ndi kulingalirabe zimene munazichita Inu.


Ndidzakondwerera ndi kusekera mwa Inu; ndidzaimbira dzina lanu, Wam'mwambamwamba Inu.


Potero udzadziwa kuti nzeru ili yotero m'moyo wako; ngati waipeza padzakhala mphotho, ndipo chiyembekezo chako sichidzalephereka.


ndipo mzimu wanga wakondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,


Kondwerani mwa Ambuye nthawi zonse: ndibwerezanso kutero, kondwerani.


Ndipo ndinatenga kabuku m'dzanja la mngelo, ndipo ndinakadya; ndipo kanali m'kamwa mwanga kozuna ngati uchi; ndipo pamene ndinakadya m'mimba mwanga mudawawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa