Masalimo 87:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo adzanena za Ziyoni, uyu ndi uyo anabadwa m'mwemo; ndipo Wam'mwambamwamba ndiye adzaukhazikitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo adzanena za Ziyoni, uyu ndi uyo anabadwa m'mwemo; ndipo Wam'mwambamwamba ndiye adzaukhazikitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma ponena za Ziyoni adzati, “Onse adabadwira kumeneko,” chifukwa Wopambanazonse mwini wake ndiye amene adzaulimbitsa mzindawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.” Onani mutuwo |