Masalimo 26:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti chifundo chanu chili pamaso panga; ndipo ndayenda m'choona chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti chifundo chanu chili pamaso panga; ndipo ndayenda m'choona chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chikondi chanu chimanditsogolera, ndipo ndimakhala wokhulupirika kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse, ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse. Onani mutuwo |