Masalimo 26:2 - Buku Lopatulika2 Mundiyesere, Yehova, ndipo mundisunthe; yeretsani impso zanga ndi mtima wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mundiyesere, Yehova, ndipo mundisunthe; yeretsani impso zanga ndi mtima wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mundiyang'anitsitse, Inu Chauta, ndi kundiyesa. Muwone mtima wanga pamodzi ndi maganizo anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni, santhulani mtima wanga ndi maganizo anga; Onani mutuwo |