Masalimo 26:4 - Buku Lopatulika4 Sindinakhala pansi ndi anthu achabe; kapena kutsagana nao anthu othyasika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Sindinakhala pansi ndi anthu achabe; kapena kutsagana nao anthu othyasika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Sindikhala pamodzi ndi anthu onyenga, sindiyenda ndi anthu achiphamaso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo, kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso. Onani mutuwo |