Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 26:5 - Buku Lopatulika

5 Ndidana nao msonkhano wa ochimwa, ndipo sindidzakhala nao pansi ochita zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndidana nao msonkhano wa ochimwa, ndipo sindidzakhala nao pansi ochita zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndimadana ndi anthu ochita zoipa, sindikhala pamodzi ndi anthu oipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 26:5
6 Mawu Ofanana  

Wodala munthuyo wosayenda mu uphungu wa oipa, kapena wosaimirira m'njira ya ochimwa, kapena wosakhala pansi pa bwalo la onyoza.


Ndikwiya nao iwo akusamala zachabe zonama, koma ndikhulupirira Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa