Masalimo 26:6 - Buku Lopatulika6 Ndidzasamba manja anga mosalakwa; kuti ndizungulire guwa la nsembe lanu, Yehova; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndidzasamba manja anga mosalakwa; kuti ndizungulire guwa la nsembe lanu, Yehova; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndimasamba m'manja kuwonetsa kuti sindidachimwe, ndimakupembedzani pa guwa lanu lansembe, Inu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga ndi kupita kukatumikira pa guwa lanu la nsembe, Inu Yehova, Onani mutuwo |