Masalimo 26:7 - Buku Lopatulika7 kuti ndimveketse mau a chiyamiko, ndi kulalikira ntchito zanu zonse zozizwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 kuti ndimveketse mau a chiyamiko, ndi kulalikira ntchito zanu zonse zozizwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndimaimba molimbika nyimbo yothokozera, ndimalalika ntchito zanu zonse zodabwitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 kulengeza mofuwula za matamando anu ndi kuwuza onse za ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwo |