Masalimo 48:8 - Buku Lopatulika8 Monga tidamva, momwemo tidapenya m'mzinda wa Yehova wa makamu, m'mzinda wa Mulungu wathu, Mulungu adzaukhazikitsa kunthawi yamuyaya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Monga tidamva, momwemo tidapenya m'mudzi wa Yehova wa makamu, m'mudzi wa Mulungu wathu, Mulungu adzaukhazikitsa kunthawi yamuyaya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Zimene ife tidazimva, taziwona zomwezo mu mzinda wa Chauta Wamphamvuzonse, mzinda wa Mulungu wathu, umene adaukhazikitsa mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya. Onani mutuwo |