Masalimo 48:7 - Buku Lopatulika7 Muswa zombo za ku Tarisisi ndi mphepo ya kum'mawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Muswa zombo za ku Tarisisi ndi mphepo ya kum'mawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu Mulungu mudaŵaononga, monga momwe mphepo yakuvuma ija imapasulira zombo zopita ku Tarisisi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa. Onani mutuwo |