Masalimo 48:6 - Buku Lopatulika6 Pomwepo anagwidwa nako kunthunthumira; anamva chowawa, ngati wam'chikuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pomwepo anagwidwa nako kunthunthumira; anamva chowawa, ngati wam'chikuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adanjenjemera koopsa, ndipo adamva ululu wonga wa mkazi wovutika pa nthaŵi yochira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira. Onani mutuwo |