Masalimo 48:10 - Buku Lopatulika10 Monga dzina lanu, Mulungu, momwemo lemekezo lanu ku malekezero a dziko lapansi; m'dzanja lamanja lanu mudzala chilungamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Monga dzina lanu, Mulungu, momwemo lemekezo lanu ku malekezero a dziko lapansi; m'dzanja lamanja lanu mudzala chilungamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Inu Mulungu, anthu amakutamandani ponseponse, monga dzina lanu latchuka pa dziko lonse lapansi. Dzanja lanu lamphamvu limapambana nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo. Onani mutuwo |