Masalimo 48:11 - Buku Lopatulika11 Likondwere phiri la Ziyoni, asekere ana aakazi a Yuda, chifukwa cha maweruzo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Likondwere phiri la Ziyoni, asekere ana akazi a Yuda, chifukwa cha maweruzo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu okhala mu Ziyoni akondwe. A ku Yuda asangalale chifukwa cha kaweruzidwe kanu kolungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu. Onani mutuwo |