Ndiloleni, Yehova, indetu ndine mtumiki wanu; ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; mwandimasulira zondimanga.
Masalimo 18:1 - Buku Lopatulika Ndikukondani, Yehova, mphamvu yanga. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndikukondani, Yehova, mphamvu yanga. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Ndimakukondani Chauta, Inu mphamvu zanga. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Davide anati: Ine ndimakukondani Inu Yehova, mphamvu zanga. |
Ndiloleni, Yehova, indetu ndine mtumiki wanu; ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; mwandimasulira zondimanga.
Pakutitu, Davide, m'mene adautumikira uphungu wa Mulungu m'mbadwo mwake mwa iye yekha, anagona tulo, naikidwa kwa makolo ake, naona chivundi;
olimbikitsidwa m'chilimbiko chonse, monga mwa mphamvu ya ulemerero wake, kuchitira chipiriro chonse ndi kuleza mtima konse pamodzi ndi chimwemwe,
Ndipo Mosetu anali wokhulupirika m'nyumba yake yonse, monga mnyamata, achitire umboni izi zidzalankhulidwazi;