Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Yohane 4:19 - Buku Lopatulika

19 Tikonda ife, chifukwa anayamba Iye kutikonda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Tikonda ife, chifukwa anayamba Iye kutikonda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye adayamba kutikonda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye anayamba kutikonda.

Onani mutuwo Koperani




1 Yohane 4:19
9 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake, ndinena kwa iwe, Machimo ake, ndiwo ambiri, akhululukidwa; chifukwa anakonda kwambiri; koma munthu amene anamkhululukira pang'ono, iye akonda pang'ono.


Inu simunandisankhe Ine, koma Ine ndinakusankhani inu, ndipo ndinakuikani, kuti mukamuke inu ndi kubala chipatso, ndi kuti chipatso chanu chikhale; kuti chimene chilichonse mukapempha Atate m'dzina langa akakupatseni inu.


Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi kotero, kuti anapatsa Mwana wake wobadwa yekha, kuti yense wakukhulupirira Iye asatayike, koma akhale nao moyo wosatha.


Koma chipatso cha Mzimu ndicho chikondi, chimwemwe, mtendere, kuleza mtima, chifundo, kukoma mtima, chikhulupiriro,


Umo muli chikondi, sikuti ife tinakonda Mulungu, koma kuti Iye anatikonda ife, ndipo anatuma Mwana wake akhale chiombolo chifukwa cha machimo athu.


Munthu akati, kuti, Ndikonda Mulungu, nadana naye mbale wake, ali wabodza: pakuti iye wosakonda mbale wake amene wamuona, sangathe kukonda Mulungu amene sanamuone.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa