1 Yohane 4:19 - Buku Lopatulika19 Tikonda ife, chifukwa anayamba Iye kutikonda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Tikonda ife, chifukwa anayamba Iye kutikonda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye adayamba kutikonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye anayamba kutikonda. Onani mutuwo |