Masalimo 36:1 - Buku Lopatulika1 Cholakwa cha woipayo chimati m'kati mwa mtima wanga, palibe kuopa Mulungu pamaso pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Cholakwa cha woipayo chimati m'kati mwa mtima wanga, palibe kuopa Mulungu pamaso pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Uchimo umalankhula mu mtima wa munthu wosamvera Mulungu. Alibe mantha ndi Mulungu m'maganizo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uthenga uli mu mtima mwanga wonena za kuchimwa kwa munthu woyipa: Mu mtima mwake mulibe kuopa Mulungu. Onani mutuwo |