Masalimo 36:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti adzidyoletsa yekha m'kuona kwake, kuti anthu sadzachipeza choipa chake ndi kukwiya nacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti adzidyoletsa yekha m'kuona kwake, kuti anthu sadzachipeza choipa chake ndi kukwiya nacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Amadzinyenga m'maganizo mwake, kotero kuti tchimo lake sangathe kulizindikira ndi kudana nalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri, sazindikira kapena kudana ndi tchimo lake. Onani mutuwo |