Masalimo 36:3 - Buku Lopatulika3 Mau a pakamwa pake ndiwo opanda pake ndi onyenga, waleka kuzindikira ndi kuchita bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mau a pakamwa pake ndiwo opanda pake ndi onyenga, waleka kuzindikira ndi kuchita bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mau a pakamwa pake ndi oipa ndi onyenga. Sachita zanzeru kapena zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo; iyeyo waleka kukhala wanzeru ndi kuchita zabwino. Onani mutuwo |